Mawu a M'munsi
b Josephus akunena kuti: “Pamene Titus analoŵamo anadabwa ndi kulimba kwake kwa mzindawo . . . Anadzuma momveka kuti: ‘Mulungu anali kumbali yathu; Mulungu ndiye amene wagwetsera Ayudawa pansi kuchokera m’malinga ameneŵa; pakuti manja a munthu kapena zida zikanachitanji pa nsanja zimenezi?’”