Mawu a M'munsi
a Nthaŵi zina munthu angapemphedwe kufufuzidwa maganizo, mwinamwake pamene akufuna kuloŵa ntchito yapamwamba. Kaya munthuyo alola kufufuzidwa kumeneku kapena ayi nchosankha chaumwini, koma ziyenera kudziŵidwa kuti kufufuza maganizo sindiko kuchiritsa maganizo.