Mawu a M'munsi
c Matenda ena amaganizo amaoneka kuti amamva mankhwala oyenera. Koma mankhwala ameneŵa ayenera kugwiritsiridwa ntchito mosamala moyang’aniridwa ndi asing’anga kapena akatswiri a nthenda zamaganizo aluso ndi achidziŵitso amene amagwiritsira ntchito mankhwala, popeza pangakhale zotulukapo zina zoipa kwambiri ngati saperekedwa pamlingo woyenera.