Mawu a M'munsi
a Pakati pa mizinda yofunika koposa ya Makedoniya, Filipi anali mudzi wotukuka wa asilikali wolamuliridwa ndi jus italicum (Lamulo Lachitaliyana). Lamulo limeneli linapatsa Afilipi zoyenera zolingana ndi zija zimene nzika za Roma zinali nazo.—Machitidwe 16:9, 12, 21.