Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Imodzi ya ntchito zazikulu za mzimu wa Mulungu pa Akristu a m’zaka za zana loyamba inali kuwadzoza monga ana olera auzimu a Mulungu ndi abale a Yesu. (2 Akorinto 1:21, 22) Zimenezi zimangochitika kwa ophunzira a Kristu okwanira 144,000. (Chivumbulutso 14:1, 3) Lerolino, Akristu ochuluka apatsidwa chiyembekezo cha moyo wosatha padziko lapansi la paradaiso. Ngakhale kuti sali odzozedwa, iwonso amalandirako chithandizo ndi chitonthozo cha mzimu woyera wa Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena