Mawu a M'munsi
a Nsanja ya Olonda ya January 1, 1995, tsamba 26, inasimba chokumana nacho cha mwana wamkazi wa Rwakabubu, Deborah, amene pemphero lake linalasa mtima gulu la asilikali achihutu ndipo linapulumutsa banjalo kuti lisaphedwe.
a Nsanja ya Olonda ya January 1, 1995, tsamba 26, inasimba chokumana nacho cha mwana wamkazi wa Rwakabubu, Deborah, amene pemphero lake linalasa mtima gulu la asilikali achihutu ndipo linapulumutsa banjalo kuti lisaphedwe.