Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

c Nyimbo zina m’buku lathu latsopano la nyimbo, Imbirani Yehova Zitamando, zili ndi mbali zinayi zogwirizana kuti awo amene amatha kuimba tchuni chosiyanacho asangalale nazo. Komabe, nyimbo zambiri azilinganiza kuti zizitsagana ndi piyano ndipo kaimbidwe kake kanakonzedwa kuti zikhalebe ndi tchuni chake cha kumaiko kumene zinachokera. Kudzikonzera manotsi m’nyimbo zolembedwa popanda mbali zake zinayi za tchuni kungachititse kuimba kwathu kumveka kokoma pamisonkhano.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena