Mawu a M'munsi
a Nkhani ya Marko yawonjezera kuti mwana wa buluyo anali “amene palibe munthu anakhalapo kale lonse.” (Marko 11:2) Mwachionekere, nyama yomwe sinagwiritsiridwepo ntchito inali yoyenerera zochitika zopatulika.—Yerekezerani ndi Numeri 19:2; Deuteronomo 21:3; 1 Samueli 6:7.