Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pano Titus anali kudzapambana basi. Komabe, pazinthu ziŵiri zazikulu, sanakwaniritse cholinga chake. Anawapatsa mwaŵi woti angogonja nadzipereke mwamtendere, koma atsogoleri a mzindawo anakana kwa mtu wa galu. Ndipo pamene makoma a mzindawo anagumulidwa potsirizira pake, analamula kuti kachisi atsale. Koma anatenthedwa yense! Ulosi wa Yesu unasonyeza bwino lomwe kuti Yerusalemu adzasakazidwa ndi kuti kachisi wake adzawonongedwa kotheratu.​—Marko 13:1, 2.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena