Mawu a M'munsi
a The New Encyclopædia Britannica imanena kuti, “kubadwanso m’moyo wina” kumatanthauza kuti “mzimu wa munthu umabadwanso m’moyo umodzi kapena yambiri yotsatizana, monga munthu, nyama, ngakhale chomera nthaŵi zina.” Liwulo “kubadwanso m’moyo wina” limagwiranso ntchito kufotokoza zimenezi, koma ambiri amangoti “munthu akafa amabadwanso kwina.” Madikishonale ambiri m’zinenero za ku India amagwiritsira ntchito mawu onse aŵiriwo.