Mawu a M'munsi
b Mtundu wina wa liwu lachigiriki lotembenuzidwa panopa kuti “ogwidwa,” pheʹro, wagwiritsidwa ntchito pa Machitidwe 27:15, 17 kufotokoza chombo chotengeka ndi mphepo. Choncho mzimu woyera ‘unawongola njira’ ya olemba Baibulo. Unawasonkhezera kusiya chidziŵitso chonyenga ndi kuikamo kokha choona.