Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ma Baibulo ena panopa amapereka lingaliro lakuti wokhudza anthu a Mulungu amakhudza, osati diso la Mulungu, koma la Israyeli kapena ngakhale lake iye mwini. Kuphonya kumeneku kunakhalako chifukwa alembi a m’nyengo zapakati amene, poyesa mosokera kukonza mavesi amene iwo anaganiza kuti sanali kupereka ulemu, anasintha vesili. Motero iwo anabisa mphamvu ya chifundo chake cha Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena