Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nkhani ino ikunena kwambiri za zinenero zomwe zingafotokoze bwino lomwe nkhaniyi koma otembenuza a zinenerozo amalekera dala kutero. Chifukwa cha kuchepa kwa mawu m’zinenero zina, otembenuza amalephera kuchita zambiri. Choncho, alangizi oona mtima achipembedzo adzafotokoza kuti ngakhale kuti wotembenuza anagwiritsira ntchito mawu osiyanasiyana kapena ngakhale kuti anagwiritsira ntchito liwu lokhala ndi matanthauzo ena osakhala a m’Malemba, liwu la m’chinenero choyambirira, neʹphesh, limagwira ntchito kwa anthu ndi nyama zomwe ndipo limatanthauza chinthu chimene chimapuma, kudya, ndipo chimene chingafe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena