Mawu a M'munsi
a Popeza kuti Matiya analoŵa m’malo mwa Yudase monga mtumwi, dzina lake—osati la Paulo—liyenera kuti linaonekera pakati pa maziko 12 amenewo. Ngakhale kuti Paulo anali mtumwi, iye sanali mmodzi wa 12 amenewo.
a Popeza kuti Matiya analoŵa m’malo mwa Yudase monga mtumwi, dzina lake—osati la Paulo—liyenera kuti linaonekera pakati pa maziko 12 amenewo. Ngakhale kuti Paulo anali mtumwi, iye sanali mmodzi wa 12 amenewo.