Mawu a M'munsi
b Paulendowu wobwerera ku Kolose, mwachionekere Onesimo ndi Tukiko anapatsidwa makalata atatu a Paulo, amene tsopano anaphatikizidwa m’mabuku ovomerezedwa a Baibulo. Kuwonjezera pa kalatayi yopita kwa Filemoni, makalata ameneŵa a Paulo anali opita kwa Aefeso ndi kwa Akolose.