Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Chidonati chinali gulu la mpatuko “lachikristu” m’zaka za zana lachinayi ndi lachisanu C.E. Akhulupiriri ake ankati makhalidwe abwino a mtumikiyo ndiwo amapangitsa masakalamenti kukhala oona ndi kuti anthu amachimo aakulu ayenera kuchotsedwa m’tchalitchi. Chiariani chinali gulu “lachikristu” m’zaka za zana lachinayi lomwe silinkavomereza umulungu wa Yesu Kristu. Arius anaphunzitsa kuti Mulungu sanabadwe ndipo alibe chiyambi. Mwana, popeza kuti anabadwa, sangakhale Mulungu monga Atate alili. Mwana sanakhalepo nthaŵi zonse koma kuti analengedwa ndipo ali ndi moyo chifukwa cha chifuniro cha Atate.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena