Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pamene anali m’ndende kachiŵiri ku Roma, Paulo anapempha Timoteo kuti abweretse “mabuku, makamaka zikopa zija zolembedwa.” (2 Timoteo 4:13) Paulo ayenera kuti anali kufuna zigawo za Malemba Achihebri kuti aziwaphunzira m’ndendemo. Mawu akuti “makamaka zikopa zija zolembedwa” angasonyeze kuti panali mabuku agumbwa ndi azikopa omwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena