Mawu a M'munsi
a Dzina lakuti Yehova limapezeka nthaŵi zoposa 7,000 m’Malemba Opatulika; onani nkhani yakuti “Kuthetsa Chinsinsi cha Dzina Lalikulu Koposa” ya mu Nsanya ya Olonda ya November 1, 1993, masamaba 3-5, yofalitsidwa ndi Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania.