Mawu a M'munsi
b Talmud ya ku Palestina imadziŵika kwambiri ndi dzina lakuti Talmud ya ku Yerusalemu. Komabe, dzina limeneli nlosayenerera, chifukwa chakuti Ayuda sanali kuloledwa kuloŵa m’Yerusalemu kwanthaŵi yaitali imene a Amoraim anakhalapo.
b Talmud ya ku Palestina imadziŵika kwambiri ndi dzina lakuti Talmud ya ku Yerusalemu. Komabe, dzina limeneli nlosayenerera, chifukwa chakuti Ayuda sanali kuloledwa kuloŵa m’Yerusalemu kwanthaŵi yaitali imene a Amoraim anakhalapo.