Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ofufuza ena amanena kuti Yuda anali kugwira mawu buku lopanda umboni lotchedwa kuti Buku la Enoke. Komabe, R. C. H. Lenski akuti: “Tikufunsa kuti: ‘Kodi buku lankhani zosiyanasiyana limeneli, Buku la Enoke, linachokera kuti?’ Buku limeneli linangosonkhanitsa nkhani zosiyanasiyana, ndipo palibe amene angatsimikizire za madeti a zigawo zake zosiyanasiyana . . . ; palibe amene ali ndi umboni wakuti mawu ake ena sanatengedwe kwa Yuda iye mwini.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena