Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngakhale kuti Paulo ‘analangiza,’ sizikutanthauza kuti anaika malamulo ake oti aliyense adziwatsatira. M’malo mwake, Paulo anali kungoyang’anira zoperekazo, zochokera kumipingo ingapo. Ndiponso, Paulo ananena kuti aliyense ‘payekha’ anafunikira kupereka “monga momwe anapindula.” M’mawu ena, chopereka chilichonse chinayenera kuperekedwa ndi munthu kwayekha ndiponso modzifunira. Palibe amene anakakamizidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena