Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Agalatiya 2:3 amanena kuti Tito anali Mhelene (Helʹlen). Zimenezi zingatanthauze kuti makolo ake anali Agiriki. Komabe, ena amati olemba Chigiriki ena ankagwiritsa ntchito liwu lochulukitsa zinthu (Helʹle·nes) ponena za anthu osakhala Agiriki amene anali Agiriki chifukwa cha chinenero ndi chikhalidwe chawo. Nzotheka kuti Tito anali Mgiriki m’lingaliro limeneli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena