Mawu a M'munsi
b Tiyenera kukumbukira kuti pamene kukwaniritsidwa kwa mawu a Yesu mu 66-70 C.E. kungatithandize kumvetsa mmene adzakwaniritsidwira pachisautso chachikulu, kukwaniritsidwa kuŵiri kumeneku sikungafanane ndendende chifukwa chakuti kukuchitika m’mikhalidwe yosiyana.