Mawu a M'munsi
a Mishnah ndi buku la ndemanga zowonjezera pa malamulo a m’Malemba, zozikidwa pa ziphunzitso za arabi (aphunzitsi) otchedwa Tannaim. Linalembedwa chakumapeto kwa zaka za zana lachiŵiri ndi kumayambiriro kwa zaka za zana lachitatu C.E.