Mawu a M'munsi
a M’madera ena, makolo ndiwo amapangabe mapangano a ukwati a ana awo. Zimenezi zingachitike aŵiriwo asanafike pa misinkhu yoti n’kukwatirana. Panthaŵiyi, anawo amaonedwa kukhala otomerana, kapena olonjezedwa kukwatirana, koma sindiko kuti akwatirana.