Mawu a M'munsi
c Katswiri wina wodziŵa Baibulo anati: “Nthaŵi zina zimachitika kuti wolakwa amamvetsera kwambiri aŵiri kapena atatu enawo (makamaka ngati ndi anthu olemekezeka) kusiyana ndi munthu mmodzi, makamaka ngati munthuyo ndi amene wasiyana naye maganizo.”