Mawu a M'munsi
a Chosangalatsa n’chakuti, chikuto cha Baibulo la Malifarensi la mu 1971 la New American Standard Bible linanenanso chimodzimodzi kuti: “Sitinagwiritse ntchito dzina la katswiri aliyense kaamba ka umboni kapena kuti ayamikiridwe chifukwa chikhulupiriro chathu n’chakuti Mawu a Mulungu ayenera kudziimira paokha.”