Mawu a M'munsi
c Popeza kuti anthu ambiri amatha kulankhula zinenero ziŵiri, tili ndi chikhulupiriro kuti Baibulo lonse kapena zigawo zake, latembenuzidwa m’zinenero zokwanira zoti n’kuŵerengedwa ndi 90 peresenti ya anthu a padziko lonse lapansi.
c Popeza kuti anthu ambiri amatha kulankhula zinenero ziŵiri, tili ndi chikhulupiriro kuti Baibulo lonse kapena zigawo zake, latembenuzidwa m’zinenero zokwanira zoti n’kuŵerengedwa ndi 90 peresenti ya anthu a padziko lonse lapansi.