Mawu a M'munsi
a Liwu lakuti “wachilendo” linali kugwiritsidwa ntchito ponena za omwe analeka kuchita zinthu mogwirizana ndi Lamulo ndipo potero akumadziika okha kutali ndi Yehova. Choncho, mkazi wachigololo, osati munthu wakudziko lina, akutchedwa “mkazi wachilendo.”