Mawu a M'munsi
a Mfundo yonena kuti zolengedwa zauzimu zimasonkhezeredwa ndi mayanjano awo imaonekera pa Chivumbulutso 12:3, 4. Pamenepo Satana akusonyezedwa kukhala “chinjoka” chimene chinagwiritsa ntchito chisonkhezero chake kuti chipangitse “nyenyezi” zinanso, kapena kuti ana aamuna auzimu, kugwirizana nacho pachipanduko chake.—Yerekezani ndi Yobu 38:7.