Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nthaŵi yomaliza pamene Yosefe akutchulidwa mwachindunji ndiyo pamene Yesu wazaka 12 zakubadwa anapezeka m’kachisi. Sizikutchulidwa kuti Yosefe analipo paphwando laukwati ku Kana, kuchiyambiyambi kwa utumiki wa Yesu. (Yohane 2:1-3) Mu 33 C.E., atapachikidwa, Yesu anapereka Mariya m’manja mwa mtumwi wake wokondedwa Yohane kuti am’samalire. Zikuoneka kuti Yesu sakanachita zimenezo zikanakhala kuti Yosefe anali adakali moyo.​—Yohane 19:26, 27.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena