Mawu a M'munsi
a M’cholembedwa chachinyengo chimenecho, wolemba wakeyo akufotokoza amene akuti ndiwo anali maonekedwe a Yesu, kuphatikizapo maonekedwe a tsitsi lake, ndevu zake, ndi maso ake. Wotembenuza Baibulo Edgar J. Goodspeed anafotokoza kuti chinyengo chimenechi “chinakonzedwa kuti anthu avomereze mafotokozedwe opezeka m’mabuku a malangizo a ojambula zithunzi onena za maonekedwe a Yesu.”