Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Monga momwe Yesu anavumbulira m’fanizo la tirigu ndi namsongole ndi m’fanizo lake la njira yotakata ndi yopapatiza (Mateyu 7:13, 14), Chikristu choona chinali kudzapitirizabe ndi anthu ochepa m’mibadwo yonse. Komabe, anthuwo sanali kudzaonekera kwambiri chifukwa cha kuchulukitsitsa kwa anthu onga namsongole, amene anali kudzadzionetsera okha ndi ziphunzitso zawo monga nkhope yeniyeni ya Chikristu. Imeneyi ndiyo nkhope imene nkhani yathu ikunena.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena