Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Nkhani inanso siyenera kunyalanyazidwa: Pa mwambo wa nacimiento ku Mexico, mwanayo amatchulidwa kuti “Mulungu Mwana” chifukwa cha malingaliro akuti anali Mulungu mwiniyo yemwe anabwera padziko lapansi monga khanda. Koma Baibulo limalongosola Yesu kukhala Mwana wa Mulungu yemwe anadzabadwa padziko lapansi; sanali Mulungu mwiniyo kapena wolingana ndi Yehova, Mulungu wamphamvuyonse. Talingalirani za zoona zake za nkhani imeneyi, zomwe zafotokozedwa pa Luka 1:35; Yohane 3:16; 5:37; 14:1, 6, 9, 28; 17:1, 3; 20:17.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena