Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Zolembedwa za Apocrypha (kutanthauza “zobisika”) ndiponso Pseudepigrapha (kutanthauza “zolembedwa zonamizira kulembedwa ndi anthu ena”) n’zolembedwa zachiyuda zoyambira m’zaka za zana lachitatu B.C.E. mpaka m’zaka za zana loyamba C.E. Tchalitchi cha Roma Katolika chimavomereza zolembedwa za Apocrypha kukhala mbali ya mabuku ouziridwa a m’Baibulo, koma Ayuda ndi Apulotesitanti sawavomereza mabuku ameneŵa. Zolembedwa za Pseudepigrapha nthaŵi zambiri zimakhala ngati kuti zikupitiriza nkhani za m’Baibulo, zolembedwa m’dzina la munthu wina wa m’Baibulo wodziŵika bwino.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena