Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngakhale kuti tsopano mtsinje wa Firate umadutsa pamtunda wa makilomita pafupifupi 16 kum’maŵa kwa malo omwe kale panali mzinda wa Uri, umboni ukusonyeza kuti kalelo mtsinjewo unkadutsa pafupi kwambiri chakumadzulo kwa mzindawo. N’chifukwa chake Abramu ankati anali wochokera “tsidya lija la mtsinje [wa Firate].”​—Yoswa 24:3.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena