Mawu a M'munsi
b Kuchita zimenezi kunali koletsedwa. Buku lina limanena kuti: “Malinga ndi malamulo pankhani ya katangale, Lex Repetundarum, munthu aliyense waudindo ankaletsedwa kulandira ziphuphu n’cholinga chilichonse kaya kuti am’mange munthu kapena kum’masula, kuweruza kapena kusaweruza, kapena kutulutsa mkaidi m’ndende.”