Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pamsonkhano wa bungwe la zipembedzo lakuti United States International Religious Freedom Commission pa November 16, 2000, mmodzi mwa anthu amene analipo anasiyanitsa anthu amene amatembenuza anthu moumiriza ndi ntchito ya Mboni za Yehova. Ananena kuti, Mboni za Yehova zikamalalikira kwa ena, zimatero mwa njira yakuti munthu atha kungoyankha kuti “sindifuna kumva uthenga wanu” n’kutseka chitseko.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena