Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yesu anagwiritsa ntchito mafanizo osiyanasiyana, ena mwa iwo anali zitsanzo, mafanizo oyerekezera chinthu china ndi chinzake, ndiponso mafanizo ofananitsa. Koma iye amatchuka n’kugwiritsa ntchito kwambiri mafanizo osimba nthano, omwe ndi “nkhani yaifupi, nthaŵi zambiri yopeka, imene munthu angaphunzirepo makhalidwe abwino kapena choonadi chauzimu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena