Mawu a M'munsi
c Malinga ndi nkhani za m’Mauthenga Abwino atatu za fanizo la Yesu, mbewu zinatsamwitsidwa ndi mavuto ndi zokondweretsa za dziko lino. Nkhanizo zimati zimenezi zinali: “Malabadiro a dziko lapansi,” “chinyengo cha chuma,” “kulakalaka kwa zinthu zina,” ndi “zokondweretsa za moyo.”—Marko 4:19; Mateyu 13:22; Luka 8:14; Yeremiya 4:3, 4.