Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Petro atapita ku Antiokeya wa ku Suriya, anacheza bwino ndi anthu okhulupirira omwe sanali Ayuda. Koma Akristu achiyuda atafika kuchokera ku Yerusalemu, Petro “anadzibweza, ndi kudzipatula yekha, pakuopa iwo a ku mdulidwe.” Tingathe kuona mmene anthu otembenuka omwe sanali Ayudawo ayenera kuti anakhumudwira pamene mtumwi wolemekezekayo anakana kudya nawo.​—Agalatiya 2:11-13.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena