Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ichi n’chifukwa china chimene anthu a ku Armenia akamaganiza za phiri la Ararati amangoona ngati lili m’dziko lawo. Kale, Armenia unali ufumu waukulu umene unkafika mpaka ku mapiri ameneŵa. N’chifukwa chake pa Yesaya 37:38, Baibulo lachigiriki la Septuagint, m’malo molemba kuti “dziko la ku Ararati” linangoti “Armenia.” Masiku ano phiri la Ararati lili m’dziko la Turkey, kufupi ndi malire ake a kummaŵa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena