Mawu a M'munsi
a Munthu wofufuza zinthu zachilengedwe dzina lake H.B. Tristram amene anapita ku madera otchulidwa m’Baibulo chapakati pa zaka za m’ma 1800 anati anapeza kuti anthu kumeneko akugwiritsabe ntchito ntchintchi za nkhuyu pothowa zithupsa.