Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nkhaŵa imene aifotokoza panoyi akuti ndiyo “nkhaŵa yobwera chifukwa cha mantha, imene imamuchotsera munthu chimwemwe chonse.” Kunena kuti “musadere nkhaŵa” kukukhala ngati zikutanthauza kuti sitiyenera kuyamba kuda nkhaŵa. Koma buku lina laumboni limati: “Verebu la Chigirikilo ndi lamulo losonyeza kuti zinthuzo zichitike nthaŵi yomwe ino, kusonyeza kulamula kuti munthu asiye kuchita chinachake chimene wayamba kale kuchichita.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena