Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M’chipululu, Aisrayeli ndiponso “anthu ambiri [osakanizika, NW]” anafunika kudya mana kuti akhale ndi moyo. (Eksodo 12:37, 38; 16:13-18) Momwemonso, Akristu onse, kaya ndi odzozedwa kapena ayi, kuti akhale ndi moyo wosatha ayenera kudya mana a kumwamba mwa kukhulupirira mphamvu zopulumutsa za thupi ndi mwazi wa Yesu zomwe zinaperekedwa nsembe.​—Onani Nsanja ya Olonda, ya February 1, 1988, masamba 30 mpaka 31.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena