Mawu a M'munsi
a Zinachitikazi zikufanana ndi nthaŵi imene mayi wa Yakobo, Rebeka, anamwetsa madzi ngamila za Eliezere. Kenako Rebeka anathamangira kumudzi kukafotokoza za kufika kwa mlendoyo. Ataona zinthu zagolide zomwe mlongo wake analandira monga mphatso, Labani anathamanga kukalandira Eliezere.—Genesis 24:28-31, 53.