Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a M’Malemba, mawu akuti “chidani” ali ndi matanthauzo angapo. Nthaŵi zina, amangotanthauza kusakonda kwambiri chinthu chinachake. (Deuteronomo 21:15, 16) Mawu akuti “chidani” nthaŵi zina amatanthauzanso kuipidwa kwambiri ndi chinthu chinachake popanda maganizo alionse ochiwononga, koma n’kumachipeŵa chifukwa chonyansidwa nacho. Koma mawu akuti “chidani” angatanthauzenso kuipidwa kwambiri ndiponso kwa nthaŵi yaitali ndi chinthu chinachake ndipo nthaŵi zambiri kophatikiza ndi dumbo. Ndi chidani chamtundu umenewu chimene tifotokoze m’nkhaniyi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena