Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mfundo zomwe zatchulidwa m’ndime ino ndi ndime yotsatira zikusonyeza miyambo ya kumayiko kwina kumene banja la mtsikana limayenera kupereka katundu kapena mphatso ku banja la mwamuna. M’mayiko ambiri ku Africa kuno mwamuna kapena banja lake ndi amene amayenera kupereka malowolo ndi mphatso ku banja la mtsikana. Komabe mfundo zimene zatchulidwazo zikukhudza miyambo iŵiri yonseyi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena