Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Buku lotchedwa La Sagrada Escritura y comentario por profesores de la Compañía de Jesús (Malemba Opatulika, Nkhani ndi Ndemanga Zolembedwa ndi Gulu la Aphunzitsi a Chipani cha Yesu) limafotokoza kuti “pakati pa Aperisi, Amedi ndi Akasidi, Anzeru a kum’mawa ndiwo anali gulu la ansembe amene ankalimbikitsa maphunziro a zamatsenga, kupenda nyenyezi komanso mankhwala.” Komabe, pofika m’zaka za m’ma 500 mpaka 1500 C.E, gulu la Anzeru a kum’mawa amene anabwera kudzaona Yesu ali mwana, anayamba kutchedwa kuti oyera ndipo anapatsidwa mayina akuti: Melchior, Gaspar, ndi Balthasar. Ndipo mafupa awo akuti amasungidwa mu tchalitchi chachikulu cha mu mzinda wa Cologne, ku Germany.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena