Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yohane, mwana wa Zebedayo, ayenera kuti analondola Yesu atakumana koyamba, ndipo anaona zina zimene Yesu anachita. Mwina ndi zimene zinachititsa Yohane kulemba zinthuzo mogwira mtima kwambiri mu Uthenga wake Wabwino. (Yohane, machaputala 2-5) Koma anadzabwererabe ku ntchito yake ya usodzi kwa nthawi ndithu Yesu asanamuitanenso.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena